Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 7:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 “‘Mwendo wakumbuyo wa kudzanja lamanja muziupereka kwa wansembe monga gawo lopatulika+ lochokera pansembe zanu zachiyanjano.

  • Levitiko 9:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Koma Aroni anaweyula*+ cha uku ndi uku ngangazo ndi mwendo wakumbuyo wa kudzanja lamanja pamaso pa Yehova, monga mmene Mose analamulira.

  • Numeri 18:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Uzitenga nyama yake kuti ikhale yako, mofanana ndi nganga ya nsembe yoweyula, komanso mwendo wam’mbuyo wakumanja.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena