Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 8:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Ndiyeno Mose anazitenga m’manja mwawo n’kuzitentha paguwa lansembe pamwamba pa nsembe yopsereza.+ Zimenezi zinali nsembe yowalongera unsembe,+ yafungo lokhazika mtima pansi.+ Inali nsembe yotentha ndi moto yoperekedwa kwa Yehova.+

  • Aefeso 5:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 ndipo yendanibe m’chikondi,+ monganso Khristu anakukondani+ n’kudzipereka yekha chifukwa cha inu. Iye anadzipereka yekha monga chopereka+ ndiponso monga nsembe yafungo lokoma kwa Mulungu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena