Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 14:39
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 39 Mose atalankhula mawuwo kwa ana onse a Isiraeli, anthu onsewo anayamba kulira kwambiri.+

  • Hoseya 7:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Sanapemphe thandizo kwa ine ndi mtima wawo wonse+ ngakhale kuti anali kulira mofuula ali pamabedi awo. Anali kungokhala, osachita chilichonse, chifukwa anali ndi chakudya chambiri ndi vinyo wambiri wotsekemera.+ Nthawi zonse anali kuchita zinthu zonditembenukira.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena