-
Ekisodo 26:37Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
37 Nsalu yotchinga khomo la chihema uipangire mizati isanu ya mtengo wa mthethe yokutidwa ndi golide. Tizitsulo tokolowekapo nsaluyo tikhale tagolide. Ndipo upange zitsulo zamkuwa zisanu zamphako zokhazikapo mizatiyo.
-