Ekisodo 10:18 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 18 Pamenepo anachoka pamaso pa Farao ndipo anapita kukachonderera Yehova.+ Yakobo 5:17 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 17 Eliya anali munthu monga ife tomwe,+ komabe anapemphera kuti mvula isagwe,+ ndipo mvula sinagwe kumeneko kwa zaka zitatu ndi miyezi 6.
17 Eliya anali munthu monga ife tomwe,+ komabe anapemphera kuti mvula isagwe,+ ndipo mvula sinagwe kumeneko kwa zaka zitatu ndi miyezi 6.