Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 9:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Koma tirigu*+ sanawonongeke, chifukwa amacha mochedwa.

  • Salimo 105:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Dzombelo linadya zomera zonse m’dziko lawo.+

      Linadyanso mbewu zonse za m’munda mwawo.

  • Yoweli 2:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Patsogolo pawo moto wawononga+ ndipo kumbuyo kwawo moto walawilawi ukunyeketsa.+ Patsogolo pawo pali dziko ngati la Edeni+ koma kumbuyo kwawo kuli chipululu chowonongeka ndipo palibe chilichonse chopulumuka.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena