Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 7:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Nyama ya nsembe zachiyanjano zoperekedwa monga nsembe yoyamikira aziidya pa tsiku limene waipereka. Asasunge iliyonse ya nyamayo kufika m’mawa.+

  • Levitiko 22:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Muziidya pa tsiku lomwelo.+ Musasiyeko iliyonse kufikira m’mawa.+ Ine ndine Yehova.

  • Deuteronomo 16:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Usapezeke ndi mtanda wa ufa wokanda wokhala ndi chofufumitsa m’dziko lako lonse masiku 7.+ Nyama iliyonse imene wapereka nsembe madzulo, pa tsiku loyamba, isagone mpaka m’mawa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena