Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 4:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 “Choncho anthu inu munayandikira ndi kuimirira m’munsi mwa phiri. Phiri limenelo linali kuyaka moto mpaka kumwamba, ndipo kunali mdima ndi mtambo wakuda.+

  • Deuteronomo 5:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 “Yehova analankhula Mawu* amenewa mokweza kumpingo wanu wonse, kuchokera pakati pa moto m’phiri,+ pamene kunachita mtambo wakuda ndi mdima wandiweyani, ndipo pa Mawuwo sanawonjezerepo kalikonse. Kenako anawalemba pamiyala iwiri yosema n’kundipatsa.+

  • Salimo 68:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Dziko lapansi linagwedezeka,+

      Kumwamba kunagwa mvula chifukwa cha inu Mulungu,+

      Phiri ili la Sinai linagwedezeka chifukwa cha inu Mulungu,+ Mulungu wa Isiraeli.+

  • Salimo 104:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Amayang’ana dziko lapansi ndipo limanjenjemera.+

      Amagwira mapiri ndipo amafuka utsi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena