Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 45:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Muyezo wa efa ndi wa mtsuko woyezera uzikhala wofanana komanso wosasinthasintha. Muyezo wa mtsuko uzikhala wokwanira gawo limodzi mwa magawo 10 a homeri.* Gawo limodzi mwa magawo 10 la muyezo wa homeri lizifanana ndi muyezo wa efa.+ Muzipeza miyezo yoyenera ya zimenezi potengera muyezo wa nthawi zonse wa homeri.

  • Hoseya 3:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Chotero ndinagula mkaziyo ndi ndalama zasiliva 15+ ndi balere wokwana muyezo umodzi wa homeri* ndi hafu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena