Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 6:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Mmodzi mwa iwo azitapako ufa wosalala wa nsembe yambewu kudzaza dzanja limodzi, ndi kutengako mafuta ake ndi lubani yense amene ali pansembe yambewuyo. Akatero, azizitentha paguwa lansembe kuti zikhale fungo la chikumbutso,+ lokhazika mtima pansi, kwa Yehova.

  • Numeri 5:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Wansembeyo azitapako nsembe yambewuyo monga chikumbutso,+ n’kuifukiza paguwa lansembe. Pambuyo pake, azipatsa mkaziyo madziwo kuti amwe.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena