Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 29:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Koma nyama ya ng’ombeyo, chikopa chake ndi ndowe zake uzitenthe ndi moto kunja kwa msasa.+ Ng’ombeyo ndi nsembe yamachimo.

  • Levitiko 1:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Nyama ya nsembe yopserezayo aziisenda chikopa ndi kuidula ziwaloziwalo.+

  • Numeri 19:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Ndiyeno ng’ombeyo itenthedwe iyeyo akuona. Atenthe chikopa chake, nyama yake, magazi ake, limodzi ndi ndowe zake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena