Ekisodo 29:8 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 8 “Ukatero utenge ana ake ndi kuwaveka mikanjo.+ Ekisodo 40:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Ndiyeno udzatenge ana ake ndi kuwaveka mikanjo.+