Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 21:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 “‘Ndipo mkulu wa ansembe wokhala pakati pa abale ake ansembe, wodzozedwa mafuta pamutu pake,+ ndi kupatsidwa mphamvu* kuti avale zovala zaunsembe,+ asalekerere tsitsi lake osalisamala+ ndipo asang’ambe zovala zake.+

  • Numeri 6:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Asadziipitse pokhudza ngakhale mtembo wa bambo ake, mayi ake, m’bale wake kapena mlongo wake, iwo akamwalira.+ Asadziipitse nawo chifukwa chizindikiro cha unaziri wake kwa Mulungu chili kumutu kwake.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena