Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 8:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Pomalizira, Mose anathira ena mwa mafuta odzozera pamutu pa Aroni ndi kum’dzoza kuti akhale wopatulika.+

  • Numeri 35:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Oweruzawo+ alanditse wakupha munthuyo m’manja mwa wobwezera magazi, ndipo am’bwezere kumzinda wothawirako kumene anathawira. Iye ayenera kukhala mumzindamo mpaka mkulu wa ansembe amene anadzozedwa ndi mafuta opatulika+ adzamwalire.

  • Salimo 133:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Zili ngati mafuta abwino amene athiridwa pamutu,+

      Amene akutsikira kundevu,

      Ndevu za Aroni,+

      Amenenso akuyenderera mpaka m’khosi la zovala zake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena