Ekisodo 22:19 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 19 “Aliyense wogonana ndi nyama aziphedwa ndithu.+ Levitiko 20:15 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 15 “‘Mwamuna akagona ndi nyama,*+ aziphedwa ndithu ndipo muziphanso nyamayo.