-
Deuteronomo 21:3Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
3 Ndipo azipeza mzinda umene uli pafupi ndi malo amene munthu wophedwayo wapezeka. Pamenepo akulu a mzinda wapafupiwo azitenga ng’ombe yaing’ono yaikazi imene sanaigwiritsepo ntchito, imene sinasenzepo goli n’kukoka chilichonse.
-