9 “‘Ndiyeno munthu wosadetsedwa awole phulusa+ la ng’ombeyo, akalithire pamalo oyera kunja kwa msasawo. Phulusalo alisunge kuti azilithira m’madzi oyeretsera+ khamu la ana a Isiraeli. Imeneyi ndi nsembe yamachimo.
23 chilichonse chimene sichingapse ndi moto,+ chidutse pamoto kuti chikhale choyera. Muchiyeretsenso ndi madzi.+ Koma chilichonse chimene chingapse ndi moto muchiyeretse ndi madzi.+