Numeri 19:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Munthu aliyense wokhudza mtembo, thupi la munthu aliyense amene angamwalire, amene sadzadziyeretsa, adzaipitsa chihema cha Yehova.+ Munthu ameneyo aphedwe kuti asakhalenso pakati pa Isiraeli.+ Iye ndi wodetsedwa chifukwa sanawazidwe madzi oyeretsera.+ Chidetso chake chikadali pa iye.+ Numeri 19:21 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 21 “‘Limeneli likhale lamulo mpaka kalekale kwa iwo, kuti munthu wowaza madzi oyeretsera, komanso munthu amene angakhudze madziwo, azichapa zovala zake.+ Akatero, azikhalabe wodetsedwa mpaka madzulo. Numeri 31:23 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 23 chilichonse chimene sichingapse ndi moto,+ chidutse pamoto kuti chikhale choyera. Muchiyeretsenso ndi madzi.+ Koma chilichonse chimene chingapse ndi moto muchiyeretse ndi madzi.+
13 Munthu aliyense wokhudza mtembo, thupi la munthu aliyense amene angamwalire, amene sadzadziyeretsa, adzaipitsa chihema cha Yehova.+ Munthu ameneyo aphedwe kuti asakhalenso pakati pa Isiraeli.+ Iye ndi wodetsedwa chifukwa sanawazidwe madzi oyeretsera.+ Chidetso chake chikadali pa iye.+
21 “‘Limeneli likhale lamulo mpaka kalekale kwa iwo, kuti munthu wowaza madzi oyeretsera, komanso munthu amene angakhudze madziwo, azichapa zovala zake.+ Akatero, azikhalabe wodetsedwa mpaka madzulo.
23 chilichonse chimene sichingapse ndi moto,+ chidutse pamoto kuti chikhale choyera. Muchiyeretsenso ndi madzi.+ Koma chilichonse chimene chingapse ndi moto muchiyeretse ndi madzi.+