Numeri 32:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 32 Tsopano ana a Rubeni+ ndi ana a Gadi+ anakhala ndi ziweto zambiri, zankhaninkhani. Iwo anayamba kusirira dziko la Yazeri+ ndi la Giliyadi, ndipo deralo linalidi malo abwino a ziweto. 1 Mbiri 6:81 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 81 mzinda wa Hesiboni+ ndi malo ake odyetserako ziweto, ndiponso mzinda wa Yazeri+ ndi malo ake odyetserako ziweto.
32 Tsopano ana a Rubeni+ ndi ana a Gadi+ anakhala ndi ziweto zambiri, zankhaninkhani. Iwo anayamba kusirira dziko la Yazeri+ ndi la Giliyadi, ndipo deralo linalidi malo abwino a ziweto.
81 mzinda wa Hesiboni+ ndi malo ake odyetserako ziweto, ndiponso mzinda wa Yazeri+ ndi malo ake odyetserako ziweto.