Numeri 26:18 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 18 Amenewa ndiwo anali mabanja a ana a Gadi. Amuna onse owerengedwa m’mabanja awo analipo 40,500.+ Yoswa 13:24 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 24 Kenako Mose anagawira dziko fuko la ana a Gadi potsata mabanja awo.+