Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 31:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Ubwino wanu,+ umene mwasungira anthu okuopani ndi wochuluka kwambiri!+

      Ubwino umenewu mwapereka kwa anthu othawira kwa inu.

      Mwaupereka kwa iwo, ana a anthu akuona.+

  • Salimo 44:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 44 Inu Mulungu, ife tamva ndi makutu athu,

      Makolo athu anatifotokozera+

      Ntchito zimene inu munachita m’masiku awo,+

      M’masiku akale.+

  • Salimo 126:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Yehova watichitira zazikulu.+

      Tasangalala.+

  • Aroma 11:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Ndithudi, madalitso amene Mulungu amapereka ndi ochuluka kwambiri.+ Nzeru+ zake n’zozama, ndiponso iye ndi wodziwa zinthu kwambiri.+ Ziweruzo zake ndi zosasanthulika,+ ndipo ndani angatulukire njira zake?

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena