Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 26:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Koma Tselofekadi, mwana wamwamuna wa Heferi, analibe ana aamuna koma aakazi okhaokha.+ Mayina a ana aakazi a Tselofekadi anali: Mala, Nowa, Hogila, Milika ndi Tiriza.+

  • 1 Mbiri 7:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Makiri anapezera akazi Hupimu ndi Supimu, ndipo dzina la mlongo wake linali Maaka.) Mwana wake wachiwiri dzina lake linali Tselofekadi,+ koma Tselofekadi anali ndi ana aakazi okhaokha.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena