Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 4:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Pamenepo Mulungu anati: “N’chiyani chimene wachitachi? Tamvera tsono. Magazi a m’bale wako akundilirira munthaka.+

  • Salimo 106:38
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 38 Choncho anali kukhetsa magazi a anthu osalakwa,+

      Magazi a ana awo aamuna ndi a ana awo aakazi,

      Amene anawapereka nsembe kwa mafano a ku Kanani.+

      Ndipo dzikolo linaipa ndi magazi amene iwo anakhetsa.+

  • Luka 11:50
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 50 N’chifukwa chake m’badwo uwu udzafunsidwa za magazi a aneneri,+ okhetsedwa kuchokera pamene dziko linakhazikika.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena