-
Levitiko 24:5Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
5 “Ndiyeno utenge ufa wosalala ndi kuphika mikate 12 yozungulira yoboola pakati. Mkate uliwonse uzipangidwa ndi ufa wokwanira magawo awiri mwa magawo 10 a muyezo wa efa.
-