Ekisodo 26:15 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 15 “Upange mafelemu oimika+ a chihema chopatulika a matabwa a mthethe. Ekisodo 36:20 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 20 Kenako anapanga mafelemu oimika a chihema chopatulika a matabwa a mthethe.+