Numeri 2:27 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 27 Kumbali yake imodzi azimangako a fuko la Aseri. Mtsogoleri wa ana a Aseri ndi Pagiyeli,+ mwana wa Okirani. Numeri 10:26 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 26 Mtsogoleri wa asilikali a fuko la ana a Aseri+ anali Pagiyeli,+ mwana wa Okirani.
27 Kumbali yake imodzi azimangako a fuko la Aseri. Mtsogoleri wa ana a Aseri ndi Pagiyeli,+ mwana wa Okirani.