Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 19:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Ndipo Yehova anauza Mose kuti: “Pita kwa anthu, uwayeretse lero ndi mawa, ndipo achape zovala zawo.+

  • Levitiko 16:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Munthu amene watentha zimenezi azichapa zovala zake ndi kusamba thupi lonse, akatero angathe kulowa mumsasa.

  • Numeri 19:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Akatha, wansembeyo achape zovala zake n’kusamba thupi lake ndi madzi. Pambuyo pake akhoza kulowa mumsasa, koma akhalebe wodetsedwa mpaka madzulo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena