Numeri 2:33 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 33 Koma Alevi sanawawerenge+ pamodzi ndi ana a Isiraeli enawo, monga Yehova analamulira Mose. Numeri 26:64 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 64 Koma pakati pa amenewa, panalibe aliyense wa amene anawerengedwa m’chipululu cha Sinai aja, pamene Mose ndi wansembe Aroni anawerenga ana a Isiraeli.+
64 Koma pakati pa amenewa, panalibe aliyense wa amene anawerengedwa m’chipululu cha Sinai aja, pamene Mose ndi wansembe Aroni anawerenga ana a Isiraeli.+