Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 3:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Uike Aroni ndi ana ake kukhala ansembe, kuti azigwira ntchito yaunsembe.+ Aliyense amene si Mlevi akayandikira malowo, aziphedwa.”+

  • Numeri 18:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Ana a Isiraeli asadzayandikirenso chihema chokumanako, kuti angadzachimwe n’kufa.+

  • 1 Samueli 6:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Chotero Mulungu anakantha anthu a ku Beti-semesi,+ chifukwa anayang’anitsitsa likasa la Yehova. Anakantha anthu 70 [[anthu 50,000]]* pakati pawo, ndipo anthu anayamba kulira chifukwa Yehova anakantha anthuwo koopsa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena