Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 4:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Aziliphimbanso ndi zikopa za akatumbu,*+ n’kuyalanso nsalu yabuluu pamwamba pake. Kenako azibwezeretsa mitengo yake yonyamulira.+

  • Numeri 4:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 “Aroni ndi ana ake akamaliza kuphimba zinthu za m’malo oyera+ ndi ziwiya zonse+ za m’malo oyerawo posamutsa msasa, ana a Kohati azilowamo n’kudzazinyamula.+ Iwo asamakhudze+ zinthu za m’malo oyerazo chifukwa angafe. Zinthu zimenezi ndizo katundu wa m’chihema chokumanako amene ana a Kohati azinyamula.+

  • Numeri 4:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Ana a Kohatiwo asadzayese kulowamo kuti akaone ngakhale pang’ono pokha zinthu zopatulikazo kuti angafe.”+

  • 1 Mbiri 13:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Pamenepo mkwiyo wa Yehova unayakira Uza, ndipo anamupha chifukwa anatambasula dzanja lake n’kugwira Likasa,+ moti Uza anafera pomwepo pamaso pa Mulungu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena