Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 2:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Ndipo zotsala za nsembe yambewu ndi za Aroni ndi ana ake,+ popeza ndi zopatulika koposa,+ zochokera pansembe zotentha ndi moto zoperekedwa kwa Yehova.

  • Levitiko 6:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Aroni ndi ana ake azidya zotsala za nsembe imeneyi.+ Azipanga mkate wopanda chofufumitsa+ ndi kudya mkatewo m’malo oyera. Aziudyera m’bwalo la chihema chokumanako.

  • Levitiko 10:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Ndiyeno Mose analankhula ndi Aroni komanso ndi Eleazara ndi Itamara, ana a Aroni amene anatsala, kuti: “Tengani nsembe yambewu+ imene yatsala pa nsembe zotentha ndi moto zoperekedwa kwa Yehova, ndipo muidye yopanda chofufumitsa pafupi ndi guwa lansembe, chifukwa nsembeyo ndi yopatulika koposa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena