Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 34:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Mwana woyamba kubadwa wa bulu muzimuwombola ndi nkhosa.+ Koma ngati simungamuwombole, muzimupha mwa kum’thyola khosi. Ndipo aliyense woyamba kubadwa mwa ana anu aamuna muzimuwombola.+ Palibe amene ayenera kuonekera kwa ine ali chimanjamanja.+

  • Levitiko 27:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Koma nyama yodetsedwa+ yoyamba kubadwa angaiwombole. Ngati munthu akufuna kuiwombola azipereka mtengo wa nyamayo n’kuwonjezerapo limodzi mwa magawo asanu a mtengowo.+ Koma ngati mwiniwake wa nyamayo saiwombola wansembe aziigulitsa pa mtengo woikidwiratu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena