Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 6:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Ansembewo akadzaliza malipenga a nyanga za nkhosa, ndipo inu mukadzamva kulira kwa malipengawo, nonse mudzafuule mfuu yankhondo mwamphamvu,+ ndipo mpanda wonse wa mzindawo udzagwa pansi.+ Pamenepo, nonsenu mudzathamangire kumeneko.”

  • Yoswa 6:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Yoswa analamula asilikaliwo+ kuti: “Musafuule kapena kulankhula kanthu, ndipo pakamwa panu pasatuluke mawu alionse kufikira tsiku limene ndidzakuuzani kuti, ‘Fuulani!’ Pamenepo mudzafuule.”+

  • 2 Mbiri 13:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Kenako amuna a Yuda anayamba kufuula mfuu ya nkhondo.+ Atafuula mfuu ya nkhondoyo, Mulungu woona anagonjetsa+ Yerobowamu ndi Aisiraeli onse pamaso pa Abiya+ ndi Ayuda.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena