Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 31:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 “Iweyo ndi wansembe Eleazara ndi atsogoleri a khamulo, mutenge zofunkha zonse, zomwe zikuphatikizapo anthu ndi ziweto.

  • Yoswa 8:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Ukachite kwa Ai ndi mfumu yake zimene unachita kwa Yeriko ndi mfumu yake.+ Koma katundu ndi ziweto za mumzindawo mukafunkhe zikakhale zanu.+ Usankhe amuna ena oti akabisale kumbuyo kwa mzindawo.”+

  • Yobu 27:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Ngakhale akonze zovalazo, wolungama ndi amene adzazivale.+

      Ndipo silivayo, wosalakwa ndi amene adzam’tenge.

  • Miyambo 13:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Munthu wabwino adzasiyira cholowa zidzukulu zake, ndipo chuma cha wochimwa chimasungidwa kuti chidzakhale cha munthu wolungama.+

  • Mlaliki 2:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Munthu wabwino pamaso pa Mulungu,+ Mulunguyo amam’patsa nzeru, kudziwa zinthu, ndi kusangalala.+ Koma wochimwa amam’patsa ntchito yotuta ndi kusonkhanitsa zinthu kuti azipereke kwa munthu amene ali wabwino pamaso pa Mulungu woona.+ Zimenezinso n’zachabechabe ndipo kuli ngati kuthamangitsa mphepo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena