Yoswa 10:8 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 8 Ndiyeno Yehova anauza Yoswa kuti: “Usawaope,+ chifukwa ndawapereka m’manja mwako.+ Palibe aliyense amene adzatha kulimbana nawe.”+ Salimo 27:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 27 Yehova ndiye kuwala+ kwanga ndi chipulumutso changa.+Ndingaopenso ndani?+Yehova ndiye malo a chitetezo cha moyo wanga.+Ndingachitenso mantha ndi ndani?+ Salimo 46:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 46 Mulungu ndiye pothawira pathu ndi mphamvu yathu,+Thandizo lopezeka mosavuta pa nthawi ya masautso.+
8 Ndiyeno Yehova anauza Yoswa kuti: “Usawaope,+ chifukwa ndawapereka m’manja mwako.+ Palibe aliyense amene adzatha kulimbana nawe.”+
27 Yehova ndiye kuwala+ kwanga ndi chipulumutso changa.+Ndingaopenso ndani?+Yehova ndiye malo a chitetezo cha moyo wanga.+Ndingachitenso mantha ndi ndani?+
46 Mulungu ndiye pothawira pathu ndi mphamvu yathu,+Thandizo lopezeka mosavuta pa nthawi ya masautso.+