Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 4:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Ansembe onyamula likasa+ la pangano la Yehova atatuluka pakati pa mtsinje wa Yorodano, ndipo mapazi+ awo ataponda kumtunda, madzi a mtsinjewo anayamba kubwerera mwakale, ndipo anasefukira+ mbali zonse ngati poyamba.

  • 1 Mbiri 12:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Awa ndi amene anawoloka mtsinje wa Yorodano+ m’mwezi woyamba* pamene mtsinjewo unasefukira mbali zake zonse.+ Kenako anathamangitsira kum’mawa ndi kumadzulo anthu onse amene anali kukhala m’zigwa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena