Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Oweruza 20:45
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 45 Chotero anatembenuka ndi kuthawira kuchipululu, kuthanthwe la Rimoni.+ Aisiraeli anapululanso ana a Benjamini 5,000 m’misewu ikuluikulu,+ ndipo anapitiriza kuwathamangitsa mpaka kukafika ku Gidomu ndi kuphanso amuna ena 2,000.

  • Oweruza 21:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ndiyeno khamu lonse linatumiza anthu kukalankhula ndi ana a Benjamini amene anali kukhala kuthanthwe la Rimoni,+ ndi kuwalonjeza mtendere.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena