-
Oweruza 5:26Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
26 Kenako anatambasula dzanja lake ndi kugwira chikhomo cha hema.
Anatambasulanso dzanja lake lamanja ndi kutenga nyundo yamtengo, ya anthu ogwira ntchito mwamphamvu.+
Atatero anakhoma Sisera m’mutu ndipo chikhomocho chinatulukira mbali ina ya mutu wakewo.+
Anaphwanya ndi kudula fupa la pafupi ndi khutu la Sisera.
-