Genesis 16:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Pambuyo pake, mngelo wa Yehova+ anakapeza Hagara m’chipululu ali pakasupe wamadzi wa panjira yopita ku Shura.+ Genesis 16:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Ndiyeno Hagara anayamba kutchula dzina la Yehova n’kunena kuti: “Inu ndinu Mulungu amene amaona chilichonse.”*+ Anatinso: “Kodi nanenso pano ndaona wotha kundionayo?” Genesis 32:24 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 24 Potsirizira pake, Yakobo anatsala yekhayekha. Kenako, munthu winawake anayamba kulimbana naye usiku wonse mpaka m’bandakucha.+ Genesis 32:30 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 30 Chotero Yakobo anatcha malowo Penieli,*+ chifukwa iye anati, “Ndaonana ndi Mulungu pamasom’pamaso, komabe ndapulumuka.”+ Oweruza 13:22 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 22 Ndiyeno Manowa anauza mkazi wake kuti: “Ife tifa basi,+ chifukwa taona Mulungu.”+ Luka 1:12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 Tsopano Zekariya anavutika mumtima ataona zimenezo, ndipo anagwidwa ndi mantha.+
7 Pambuyo pake, mngelo wa Yehova+ anakapeza Hagara m’chipululu ali pakasupe wamadzi wa panjira yopita ku Shura.+
13 Ndiyeno Hagara anayamba kutchula dzina la Yehova n’kunena kuti: “Inu ndinu Mulungu amene amaona chilichonse.”*+ Anatinso: “Kodi nanenso pano ndaona wotha kundionayo?”
24 Potsirizira pake, Yakobo anatsala yekhayekha. Kenako, munthu winawake anayamba kulimbana naye usiku wonse mpaka m’bandakucha.+
30 Chotero Yakobo anatcha malowo Penieli,*+ chifukwa iye anati, “Ndaonana ndi Mulungu pamasom’pamaso, komabe ndapulumuka.”+