Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Oweruza 7:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Tsopano Gidiyoni anafika kumsasawo ndipo anangomva munthu akusimbira mnzake zimene analota, kuti: “Tamvera zimene ndalota ine.+ Ndalota mtanda wa mkate wa balere wozungulira ukugubuduzika kubwera mumsasa wa Amidiyani. Mtandawo unafika pahema lina ndi kuliwomba moti hemalo linagwa.+ Kenako mtandawo unagadabuza hemalo n’kuliphwasula.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena