Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Oweruza 14:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Pamenepo mkazi wa Samisoni anayamba kulira pamaso pa mwamuna wake,+ ndipo ankamuuza kuti: “Umandida, sundikonda ayi.+ Iwe waphera mwambi anthu a mtundu wanga,+ koma ine sunandiuze tanthauzo lake.” Atatero anamuuza kuti: “Ndikuuze chifukwa chiyani, pamene bambo kapena mayi anga sindinawauze?”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena