Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 20:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 “Uzilemekeza bambo ako ndi mayi ako+ kuti masiku ako atalike m’dziko limene Yehova Mulungu wako akukupatsa.+

  • Ekisodo 20:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 “Usabe.+

  • Levitiko 6:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 iye akachimwa mwa njira imeneyi, ndipo wapalamuladi,+ azibweza zinthu zimene anafwambazo, kapena zinthu zimene analanda mwachinyengo, kapena chimene chili m’manja mwake chimene anam’sungitsa, kapena chinthu chotayika chimene anatola,

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena