Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 21:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Womenya abambo ake ndi mayi ake aziphedwa ndithu.+

  • Miyambo 1:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Mwana wanga, tamvera malangizo a bambo ako,+ ndipo usasiye malamulo a mayi ako,+

  • Yeremiya 35:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Ndiyeno Yeremiya anauza anthu a m’nyumba ya Rekabu kuti: “Yehova wa makamu, Mulungu wa Isiraeli wanena kuti, ‘Chifukwa chakuti mwamvera lamulo la kholo lanu Yehonadabu,+ ndipo mukupitiriza kusunga malamulo ake onse ndi kuchita zonse zimene anakulamulani,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena