Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 12:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Davide atamva zimenezi anadzuka pansi pamene anagonapo n’kukasamba ndi kudzola+ mafuta. Kenako anasintha zovala zake n’kukalowa m’nyumba+ ya Yehova ndipo anagwada n’kuweramira pansi.+ Atachoka kumeneko anakalowa m’nyumba yake ndi kupempha kuti amukonzere chakudya. Mwamsanga anam’bweretsera mkate ndipo anadya.

  • 2 Samueli 14:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Choncho Yowabu anatumiza anthu ku Tekowa+ kuti akatenge mkazi wanzeru.+ Atabwera naye, Yowabu anamuuza kuti: “Chonde ukhale ngati munthu amene ali panyengo yolira maliro, ndipo uvale zovala za panyengo yolira maliro, komanso usadzole mafuta.+ Ukatero ukhale ngati mkazi amene wakhala akulira maliro kwa masiku ambiri.+

  • Mlaliki 9:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Nthawi zonse zovala zako zizikhala zoyera,+ ndipo pamutu pako pasamasowe mafuta.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena