Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 18:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Anandilanditsa kwa mdani wanga wamphamvu,+

      Anandilanditsa kwa odana nane chifukwa anali amphamvu kuposa ine.+

  • Salimo 34:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Masoka a munthu wolungama ndi ochuluka,+

      Koma Yehova amamupulumutsa ku masoka onsewo.+

  • Yesaya 54:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Chida chilichonse chimene chidzapangidwe kuti chikuvulaze sichidzapambana,+ ndipo lilime lililonse limene lidzalimbane nawe pamlandu udzalitsutsa.+ Ichi ndi cholowa cha atumiki a Yehova,+ ndipo chilungamo chawo n’chochokera kwa ine,” akutero Yehova.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena