-
1 Mbiri 12:19Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
19 Analiponso ena a fuko la Manase amene anapanduka n’kupita kwa Davide pamene iye anabwera ndi Afilisiti+ kudzamenyana ndi Sauli. Koma Davide sanawathandize Afilisitiwo chifukwa olamulira awo ogwirizana+ atakambirana, anam’bweza chifukwa anati: “Ameneyu akhoza kukatitembenukira n’kugwirizana ndi mbuye wake Sauli, kenako akatidula mitu.”+
-