-
1 Mbiri 12:19Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
19 Panalinso anthu ena a fuko la Manase amene anapita kwa Davide pamene iye anabwera ndi Afilisiti kudzamenyana ndi Sauli. Koma Davide sanathandize Afilisitiwo chifukwa olamulira awo atakambirana,+ anamʼbweza poganiza kuti: “Ameneyu akhoza kukatitembenukira nʼkugwirizana ndi mbuye wake Sauli, nʼkutipha.”+
-