Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 23:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Nthawi yomweyo Davide ananyamuka pamodzi ndi amuna pafupifupi 600+ amene anali kuyenda naye. Iwo anatuluka mu Keila ndi kumangoyendayenda kulikonse kumene akufuna. Ndiyeno uthenga unafika kwa Sauli kuti Davide wathawa ku Keila. Sauli atamva zimenezi sanapitekonso.

  • 1 Samueli 27:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Choncho Davide pamodzi ndi amuna 600+ amene anali kuyenda naye ananyamuka ndi kupita kwa Akisi+ mfumu ya Gati, mwana wa Maoki.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena