Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 18:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Yehova ndiye thanthwe langa, malo anga achitetezo ndiponso Wopereka chipulumutso kwa ine.+

      Mulungu wanga ndiye thanthwe langa. Ine ndidzathawira kwa iye.+

      Iye ndiye chishango changa, nyanga* yanga ya chipulumutso ndiponso ndiye malo anga okwezeka achitetezo.+

  • Salimo 89:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Pakuti inu ndinu amene mumachititsa mphamvu zawo kukhala zaulemerero.+

      Ndipo mwa kukoma mtima kwanu, nyanga* yathu imakwezedwa.+

  • Salimo 92:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Koma inu mudzakweza nyanga* yanga ngati nyanga ya ng’ombe yam’tchire yamphongo.*+

      Ndidzadzola mafuta abwino.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena