Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 17:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Ndiyeno Aamaleki+ anabwera kudzamenyana ndi Isiraeli ku Refidimu.+

  • Numeri 24:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Tsopano Balamu ataona Amaleki, anapitiriza mawu ake a ndakatulo, kuti:+

      “Amaleki anali woyamba wa anthu a mitundu ina,+

      Koma chiwonongeko chake chidzakhaladi mapeto ake.”+

  • Deuteronomo 25:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 “Muzikumbukira zimene Aamaleki anakuchitirani panjira pamene munali kutuluka mu Iguputo.+

  • Deuteronomo 25:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Iwo anakumana nanu panjira ndi kupha anthu oyenda movutika m’gulu lanu amene anali kumbuyo. Iwo anachita izi pamene munali olefuka ndi otopa ndipo sanaope Mulungu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena